Amayankha lyrics by Chifundo Chikonga - original song full text. Official Amayankha lyrics, 2024 version | LyricsMode.com
Request & respond explanations
  • Don't understand the meaning of the song?
  • Highlight lyrics and request an explanation.
  • Click on highlighted lyrics to explain.
Chifundo Chikonga – Amayankha lyrics
Ho-yee mama wee! ah yeah
Ooh yeah aah mthefile
O! mama wee!

Anali kuti dzana, mtima utawawa
Nkhawa zitafika, anabwerera m'mbuyo
Analira kosatha, usiku ndi usana
Atasweka mtima m'vuto lawo
Anamuuza Yesu, atathedwa nzeru
Anayembekeza, amayankha
Anamuuza Yesu, atathedwa nzeru
Anayembekeza, amayankha

Chorus
Anamuuza Yesu (Amayankha)
Anayitanirabe (Amayankha)
Dzina la Yehova (Amayamkha)
Zonse zinasintha (Amayankha)

Amayankha... yeah ihh

Anali kuti dzana, litavuta banja
Atakhumudwitsidwa misonzi ikutsika
Anadera nkhawa ntchito itasowa
Anavomereza kuti sadzayipeza
Anamuuza Yesu, atathedwa nzeru
Anayembekeza poti amayankha
Anamuuza Yesu, atathedwa nzeru
Anayembekeza ena nkumadabwa

Chorus
Anamuuza Yesu (Amayankha)
Anayitanirabe (Amayankha)
Dzina la Yehova (Amayamkha)
Zonse zinasintha (Amayankha)

Amayankha ah oh Amayankha

Bridge

Nanga ukulira chani iwe?
Pukuta misonzi
Zabwino zidzera oh, iwo oyembekeza, ooh uohuh!

Chorus til end
×



Lyrics taken from /lyrics/c/chifundo_chikonga/amayankha.html

  • Email
  • Correct
Submitted by fundo95

Amayankha meanings

Write about your feelings and thoughts about Amayankha

Know what this song is about? Does it mean anything special hidden between the lines to you? Share your meaning with community, make it interesting and valuable. Make sure you've read our simple tips.
U
Min 50 words
Not bad
Good
Awesome!

Post meanings

U
Min 50 words
Not bad
Good
Awesome!

official video

Featured lyrics

0-9 A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z